ترجمهٔ معانی قرآن کریم - ترجمهٔ چوایی * - لیست ترجمه ها


ترجمهٔ معانی آیه: (24) سوره: سوره نحل
وَإِذَا قِيلَ لَهُم مَّاذَآ أَنزَلَ رَبُّكُمۡ قَالُوٓاْ أَسَٰطِيرُ ٱلۡأَوَّلِينَ
Ndipo (osakhulupirira) akafunsidwa: “Kodi Mbuye wanu watumizanji (kwa Mneneri Muhammad {s.a.w})?” Akunena: “(Sadatumize chilichonse koma) nthano zabodza za anthu akale.”[250]
[250] Omasulira Qur’an akunena kuti, opembedza mafano amaima m’njira zolowera mu mzinda wa Makka ndi cholinga chopatula anthu kwa Mtumiki (s.a.w). Anthu odzachita Hajj akawafunsa kuti: “Kodi nchiyani chavumbulutsidwa kwa Muhammad?” Iwo amati: “Ndi nthano zabodza za anthu akale osati mawu a Allah.”
تفسیرهای عربی:
 
ترجمهٔ معانی آیه: (24) سوره: سوره نحل
فهرست سوره ها شماره صفحه
 
ترجمهٔ معانی قرآن کریم - ترجمهٔ چوایی - لیست ترجمه ها

ترجمهٔ معانی قرآن کریم به زبان چوایی، برگردان: خالد ابراهیم بیتالا. نسخهٔ سال ۲۰۲۰ میلادی.

بستن