クルアーンの対訳 - チェワ語対訳 * - 対訳の目次


対訳 節: (24) 章: 蜜蜂章
وَإِذَا قِيلَ لَهُم مَّاذَآ أَنزَلَ رَبُّكُمۡ قَالُوٓاْ أَسَٰطِيرُ ٱلۡأَوَّلِينَ
Ndipo (osakhulupirira) akafunsidwa: “Kodi Mbuye wanu watumizanji (kwa Mneneri Muhammad {s.a.w})?” Akunena: “(Sadatumize chilichonse koma) nthano zabodza za anthu akale.”[250]
[250] Omasulira Qur’an akunena kuti, opembedza mafano amaima m’njira zolowera mu mzinda wa Makka ndi cholinga chopatula anthu kwa Mtumiki (s.a.w). Anthu odzachita Hajj akawafunsa kuti: “Kodi nchiyani chavumbulutsidwa kwa Muhammad?” Iwo amati: “Ndi nthano zabodza za anthu akale osati mawu a Allah.”
アラビア語 クルアーン注釈:
 
対訳 節: (24) 章: 蜜蜂章
章名の目次 ページ番号
 
クルアーンの対訳 - チェワ語対訳 - 対訳の目次

クルアーン・チェワ語対訳 - Khalid Ibrahim

閉じる