Firo maanaaji al-quraan tedduɗo oo - Firo siisiiwo * - Tippudi firooji ɗii


Firo maanaaji Aaya: (183) Simoore: Simoore koreeji imraan
ٱلَّذِينَ قَالُوٓاْ إِنَّ ٱللَّهَ عَهِدَ إِلَيۡنَآ أَلَّا نُؤۡمِنَ لِرَسُولٍ حَتَّىٰ يَأۡتِيَنَا بِقُرۡبَانٖ تَأۡكُلُهُ ٱلنَّارُۗ قُلۡ قَدۡ جَآءَكُمۡ رُسُلٞ مِّن قَبۡلِي بِٱلۡبَيِّنَٰتِ وَبِٱلَّذِي قُلۡتُمۡ فَلِمَ قَتَلۡتُمُوهُمۡ إِن كُنتُمۡ صَٰدِقِينَ
Amene anenanso: “Allah Adatilamula ife kuti tisakhulupirire mtumiki aliyense mpaka atabwera ndi nsembe yopserezedwa ndi moto.” Nena: “Adakudzerani atumiki ndisanadze ndi zisonyezo zooneka ndi chimene mukunenachi. Nanga bwanji mudawapha, ngati mukunenadi zoona?”[103]
[103] Ayuda pamene Mtumiki (s.a.w) amawauza kuti amtsate amanena kuti: “Ife sadatilamule kutsata Mtumiki yemwe akuloleza sadaka. Koma atilamula kutsata atumiki okhawo omwe akulamula kuti sadaka zonse azisonkhanitse pamodzi kenako azitenthe ndi moto. Kapena moto udze kudzapsereza.” Zoonadi, atumiki otero adadza koma sadawatsate monga momwe Allah wanenera apa. Komabe sanawalamule kutsata atumiki otero okhawo. Kutero nkungofuna kupeza chonamizira basi.
Faccirooji aarabeeji:
 
Firo maanaaji Aaya: (183) Simoore: Simoore koreeji imraan
Tippudi cimooje Tonngoode hello ngoo
 
Firo maanaaji al-quraan tedduɗo oo - Firo siisiiwo - Tippudi firooji ɗii

Firo maanaaji al-quraan tedduɗo oo fayde e ɗemngal siisii, fari ɗum ko Kaaliid piitalaa. Tummbutere hitaande 2020

Uddude