Traduction des sens du Noble Coran - Traduction en chewa * - Lexique des traductions


Traduction des sens Verset: (14) Sourate: SABA
فَلَمَّا قَضَيۡنَا عَلَيۡهِ ٱلۡمَوۡتَ مَا دَلَّهُمۡ عَلَىٰ مَوۡتِهِۦٓ إِلَّا دَآبَّةُ ٱلۡأَرۡضِ تَأۡكُلُ مِنسَأَتَهُۥۖ فَلَمَّا خَرَّ تَبَيَّنَتِ ٱلۡجِنُّ أَن لَّوۡ كَانُواْ يَعۡلَمُونَ ٱلۡغَيۡبَ مَا لَبِثُواْ فِي ٱلۡعَذَابِ ٱلۡمُهِينِ
Pamene tidalamula imfa yake (Sulaiman), palibe chimene chidawasonyeza za imfa yake koma kachirombo ka m’nthaka (chiswe) kamene kadadya ndodo yake. Choncho pamene adagwa, ziwanda zidazindikira kuti zikadakhala zikudziwa zobisika sizidakakhala m’chilango chosambulacho.[334]
[334] Kalelo anthu adali ndi chikhulupiliro chakuti ziwanda zimadziwa zamseri; monga kudziwa zam’tsogolo. Ndipo kudapezeka kuti Sulaiman adaimilira kupemphera ku chipinda chake chopemphelera uku atatsamira ndodo yake, imfa niimpeza ali chiimilire, choncho adakhala chaka chathunthu ali chomwecho uku atafa kale. Mmenemo nkuti ziwanda zikugwira ntchito yotopetsa, osadziwa kuti Sulaiman adafa, mpaka pamene chiswe chidadya ndodo imene adatsamira, nagwa pansi. Apo mpomwe imfa yake idadziwika. Potero anthu adadziwa tsopano kuti ziwanda sizidziwa zam’tsogolo.
Les exégèses en arabe:
 
Traduction des sens Verset: (14) Sourate: SABA
Lexique des sourates Numéro de la page
 
Traduction des sens du Noble Coran - Traduction en chewa - Lexique des traductions

Traduction des sens du noble Coran en langue chewa, par Khâlid Ibrâhîm Bîtâlâ (édition 2020).

Fermeture