Check out the new design

የቅዱስ ቁርዓን ይዘት ትርጉም - የቺቼዋኛ ትርጉም - ኻሊድ ኢብራሂም ቢታላ * - የትርጉሞች ማዉጫ


የይዘት ትርጉም ምዕራፍ: አል ዋቂዓህ   አንቀጽ:

Al-Wâqi’ah

إِذَا وَقَعَتِ ٱلۡوَاقِعَةُ
Chikadzachitika chochitikacho (Qiyâma).
የአረብኛ ቁርኣን ማብራሪያ:
لَيۡسَ لِوَقۡعَتِهَا كَاذِبَةٌ
Palibe wotsutsa za kuchitika kwake.
የአረብኛ ቁርኣን ማብራሪያ:
خَافِضَةٞ رَّافِعَةٌ
Chidzatsitsa (oipa) ndi kutukula (abwino).
የአረብኛ ቁርኣን ማብራሪያ:
إِذَا رُجَّتِ ٱلۡأَرۡضُ رَجّٗا
Nthaka ikadzagwedezeka kwamphamvu.
የአረብኛ ቁርኣን ማብራሪያ:
وَبُسَّتِ ٱلۡجِبَالُ بَسّٗا
Ndipo mapiri akadzaperedwaperedwa.
የአረብኛ ቁርኣን ማብራሪያ:
فَكَانَتۡ هَبَآءٗ مُّنۢبَثّٗا
Nkukhala fumbi longouluka.
የአረብኛ ቁርኣን ማብራሪያ:
وَكُنتُمۡ أَزۡوَٰجٗا ثَلَٰثَةٗ
Choncho, inu mudzakhala m’magulu atatu (kulingana ndi zochita zanu).
የአረብኛ ቁርኣን ማብራሪያ:
فَأَصۡحَٰبُ ٱلۡمَيۡمَنَةِ مَآ أَصۡحَٰبُ ٱلۡمَيۡمَنَةِ
Anthu akumanja (abwino;) taonani kukula kwa ulemelero wa anthu akumanja!
የአረብኛ ቁርኣን ማብራሪያ:
وَأَصۡحَٰبُ ٱلۡمَشۡـَٔمَةِ مَآ أَصۡحَٰبُ ٱلۡمَشۡـَٔمَةِ
Ndi anthu akumanzere (oipa;) taonani kuipa khalidwe la anthu akumanzere!
የአረብኛ ቁርኣን ማብራሪያ:
وَٱلسَّٰبِقُونَ ٱلسَّٰبِقُونَ
Ndipo otsogola (pochita zabwino pa dziko) adzakhalanso otsogola (polandira ulemu tsiku lachimaliziro).
የአረብኛ ቁርኣን ማብራሪያ:
أُوْلَٰٓئِكَ ٱلۡمُقَرَّبُونَ
Iwowo ndioyandikitsidwa (kwa Allah).
የአረብኛ ቁርኣን ማብራሪያ:
فِي جَنَّٰتِ ٱلنَّعِيمِ
M’minda yamtendere.
የአረብኛ ቁርኣን ማብራሪያ:
ثُلَّةٞ مِّنَ ٱلۡأَوَّلِينَ
(Iwowo oyandikitsidwawo), gulu lalikulu lochokera kumibadwo yakale.
የአረብኛ ቁርኣን ማብራሪያ:
وَقَلِيلٞ مِّنَ ٱلۡأٓخِرِينَ
Ndipo ochepa ochokera ku mbadwo wotsirizira.
የአረብኛ ቁርኣን ማብራሪያ:
عَلَىٰ سُرُرٖ مَّوۡضُونَةٖ
Uku ali m’makama (m’mabedi) olukidwa ndi zingwe zagolide,
የአረብኛ ቁርኣን ማብራሪያ:
مُّتَّكِـِٔينَ عَلَيۡهَا مُتَقَٰبِلِينَ
Atatsamira m’makamawo uku akuyang’anizana (mwachikondi).
የአረብኛ ቁርኣን ማብራሪያ:
 
የይዘት ትርጉም ምዕራፍ: አል ዋቂዓህ
የምዕራፎች ማውጫ የገፅ ቁጥር
 
የቅዱስ ቁርዓን ይዘት ትርጉም - የቺቼዋኛ ትርጉም - ኻሊድ ኢብራሂም ቢታላ - የትርጉሞች ማዉጫ

ተርጓሙ በኻሊድ ኢብራሂም ቢታላ።

መዝጋት