पवित्र कुरअानको अर्थको अनुवाद - चेवा अनुवाद * - अनुवादहरूको सूची


अर्थको अनुवाद सूरः: सूरतुत्तीन   श्लोक:

सूरतुत्तीन

وَٱلتِّينِ وَٱلزَّيۡتُونِ
Ndikulumbilira mitengo ya Mkuyu ndi Zitona (pansi pa mitengo imeneyi Ibrahim ndi Nuh (Nowa) adapeza uneneri),
अरबी व्याख्याहरू:
وَطُورِ سِينِينَ
Ndi phiri la Sinai (pamene Allah adamulankhulira Mûsa),
अरबी व्याख्याहरू:
وَهَٰذَا ٱلۡبَلَدِ ٱلۡأَمِينِ
Ndiponso mzinda uwu (wolemekezeka) wamtendere; (Makka, womwe adapatsiridwa uneneri Muhammad) (s.a.w).
अरबी व्याख्याहरू:
لَقَدۡ خَلَقۡنَا ٱلۡإِنسَٰنَ فِيٓ أَحۡسَنِ تَقۡوِيمٖ
Palibe chikaiko, tamulenga munthu mkalengedwe kabwino, kolingana (ndipo ali ndi mbiri zabwino).[457]
[457] M’gulu la nyama palibe yopambana kuposa munthu mkalengedwe ndi pa nzeru.
अरबी व्याख्याहरू:
ثُمَّ رَدَدۡنَٰهُ أَسۡفَلَ سَٰفِلِينَ
Pambuyo pake tamubwezera pansi kumposa wa pansi.[458]
[458] Munthu ali ndi makhalidwe awiri: Ngati agwiritsa ntchito nzeru zake amaongoka ndipo amaiposa nyama ili yonse. Koma ngati sagwiritsa ntchito nzeru zake amasokera ndi kukhala wapansi kuposa nyama zonse.
अरबी व्याख्याहरू:
إِلَّا ٱلَّذِينَ ءَامَنُواْ وَعَمِلُواْ ٱلصَّٰلِحَٰتِ فَلَهُمۡ أَجۡرٌ غَيۡرُ مَمۡنُونٖ
Kupatula amene akhulupirira ndikumachita zabwino, adzakhala nawo iwo malipiro osatha.
अरबी व्याख्याहरू:
فَمَا يُكَذِّبُكَ بَعۡدُ بِٱلدِّينِ
Tsono nchiyani chakuchititsa kuti ukanire kuuka ndi malipiro pambuyo (poona mphamvu zathu pa chilichonse)?[459]
[459] (Ndime 7-8) Allah akuuza munthu kuti: Pambuyo podziwa kuti Allah ndi Yemwe adapanga zimenezo, ndi chiyani nanga chikumukaikitsa za tsiku la chiweruziro?
अरबी व्याख्याहरू:
أَلَيۡسَ ٱللَّهُ بِأَحۡكَمِ ٱلۡحَٰكِمِينَ
Kodi Allah si Muweruzi wa nzeru kuposa aweruzi onse?
अरबी व्याख्याहरू:
 
अर्थको अनुवाद सूरः: सूरतुत्तीन
अध्यायहरूको (सूरःहरूको) सूची رقم الصفحة
 
पवित्र कुरअानको अर्थको अनुवाद - चेवा अनुवाद - अनुवादहरूको सूची

पवित्र कुर्आनको अर्थको चेवा भाषामा अनुवाद, अनुवादक : खालिद इब्राहीम बेताला, प्रकाशन : २०२० ।

बन्द गर्नुस्