क़ुरआन के अर्थों का अनुवाद - चेवा अनुवाद * - अनुवादों की सूची


अर्थों का अनुवाद सूरा: सूरा अत्-तकासुर   आयत:

सूरा अत्-तकासुर

أَلۡهَىٰكُمُ ٱلتَّكَاثُرُ
Kwakutangwanitsani kusonkhanitsa (chuma chambiri ndi ana).[477]
[477] (Ndime 1-2) Ndi chizolowezi cha anthu kupikisana pa chuma ndi pa ana. Choncho, mma Ayah awa: 1-2 Allah akuwauza: Kupikisana kwawo kochuluka, kukonda za m’dziko kwambiri, kwaiwalitsa kutumikira Allah mpaka imfa kuwapeza.
अरबी तफ़सीरें:
حَتَّىٰ زُرۡتُمُ ٱلۡمَقَابِرَ
Mpakana mwapita kumanda (mwamwalira ndikukalowa m’manda).
अरबी तफ़सीरें:
كَلَّا سَوۡفَ تَعۡلَمُونَ
Sichoncho! Mudziwa posachedwapa.[478]
[478] Tanthauzo lake ndilakuti, pamene idzakufikirani imfa mudzadziwa kuti mudali kutaya nthawi ndi zinthu zopanda pake.
अरबी तफ़सीरें:
ثُمَّ كَلَّا سَوۡفَ تَعۡلَمُونَ
Ndiponso sichoncho! Mudziwa posachedwapa.
अरबी तफ़सीरें:
كَلَّا لَوۡ تَعۡلَمُونَ عِلۡمَ ٱلۡيَقِينِ
Sichoncho! mukadakhala mukudziwa, kudziwa kwachitsimikizo (sibwenzi mukutangwanika ndi za mdziko).
अरबी तफ़सीरें:
لَتَرَوُنَّ ٱلۡجَحِيمَ
Ndithudi mudzauona Moto.
अरबी तफ़सीरें:
ثُمَّ لَتَرَوُنَّهَا عَيۡنَ ٱلۡيَقِينِ
Kenako mudzauona ndithu ndi diso lachitsimikizo.
अरबी तफ़सीरें:
ثُمَّ لَتُسۡـَٔلُنَّ يَوۡمَئِذٍ عَنِ ٱلنَّعِيمِ
Tsono patsikulo ndithudi mudzafunsidwa za mtendere (omwe munapatsidwa).[479]
[479] Munthu aliyense ndi chilichonse chimene ali nacho ndi mphatso yochokera kwa Allah. Choncho, pa tsiku lachimaliziro adzafunsidwa za momwe adagwiritsira ntchito mphatso zimenezi, kaya m’njira yoipa kapena yabwino.
अरबी तफ़सीरें:
 
अर्थों का अनुवाद सूरा: सूरा अत्-तकासुर
सूरों की सूची पृष्ठ संख्या
 
क़ुरआन के अर्थों का अनुवाद - चेवा अनुवाद - अनुवादों की सूची

पवित्र क़ुरआन के अर्थों का चेवा अनुवाद। अनुवाद ख़ालिद अबराहीम बेताला ने किया है। प्रति वर्ष 2020 ईसवी।

बंद करें